Home » Lyrics » Praise Pemphero Kambela_Sindidzapembedza_Lyrics

Praise Pemphero Kambela_Sindidzapembedza_Lyrics

by Harris Msosa
564 views

Verse 1

Mam’mawa, masana, madzulo,
Simusintha muli yemweyo
Khutu lanu silogontha
Kuti mungalephere kundimva
Mkono wanu siwawufupi
Kuti mulephere kukhudza
Maso anu si akhungu
Kuti mulephere kupenya
Pali timilungu tina
tomwe anthu amapembedza
Maso ato ndi akhungu
Sitingathe kuwapenya
Tili ndi makutu inde
Sitingathe ku wamva
Tili ndi manja inde sitingathe kuwa pulumutsa

Chorus

Sindi dzapembedza
milungu ina
Koma inu Mulungu wamoyo

Verse 2

Mene mumkalenga dzikoli
Munali napo pokhala
Mene mumkalenga kumwamba malo anu analipo
Mene mkalenga nyanja
Mene mumkalenga mapiri
Mene mumkalenga Munthu
Munalenga ndi mawu anu
Munati tilenge Munthu
Nchifaniziro chathu
Chifanizo cha inu
Tate, mwana ndi Mzimu woyera

Chorus

Sindi dzapembedza
milungu ina
Koma inu Mulungu wamoyo

Follow Us

More Songs From Praise pemphero

malawigospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel Music and any gospel News.malawigospelmusic.com offer services like song lyrics,Audio upload,poems,Music video upload on our You Tube channel called Malawian Gospel Music, Artist biography, Extended playlist (EP),Article, Album and Banner on website. For inquiry contact these numbers 0888 069 117/0885 572 836 or 0983 592 032/0994 56 15 46 or info@malawigospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media