Home » Lyrics » Praise Pemphero Kambela_Mwayenera_Lyrics

Praise Pemphero Kambela_Mwayenera_Lyrics

by Harris Msosa
629 views

Verse 1

Ndina sochela kutali,
Ine ndinadya ndi nguluwe,
Moyo wanga ine unatayika,
Koma Ambuye munandigwira dzanja.

Chorus

Mwayenela,
Mwayenela,
Mwayenela,
Ndinu chipulumutso changa.

Verse 2

Satana amakondwa,
Akandiona kuti ndagwa,
Popeza amadziwa
Kuti wagonjetsa,
Kwake ndi kuba, kupha ndi kuwononga.

Chorus
Mwayenela,
Mwayenela,
Mwayenela,
Ndinu chipulumutso changa.

Follow Us

More Songs From Praise pemphero

malawigospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel Music and any gospel News.malawigospelmusic.com offer services like song lyrics,Audio upload,poems,Music video upload on our You Tube channel called Malawian Gospel Music, Artist biography, Extended playlist (EP),Article, Album and Banner on website. For inquiry contact these numbers 0888 069 117/0885 572 836 or 0983 592 032/0994 56 15 46 or info@malawigospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media