Home » Lyrics » Loyce Yotamu – Odala Lyrics

Loyce Yotamu – Odala Lyrics

by Malawi Gospel Music
518 views

Chorus

Ndiwe Odala Odala Odala Odala x 4

Verse 1

Kaya waphinjika usataye mtima yesu wamoyo ali pa mbari pako

Nyengo zathina usandaure itana mbuyeyesu adzakuyankha

Wasowa chakudya usandaure kuti udzadya chan itana yesu

Ukusowa mwana usandaure kumbuka Hanna nae Nyengo zake

Ukusowa banja lowa nchipinda chako pinda bondo lako ambuye akumva

Ndiwe lova pemphera Sala kudya Mulungu omva tseli adzakuyankha

Kumbukira sachedwa safulumira mu nthawi yoyikika iye adzayankha

Tikapemphera kulibe Nyengo zomwe zingamulake iye adzayankha.

Chorus

Verse 2

Dziko limanyoza ili dziko limatodza ili dziko limaweluza

Koma Kumbukira chouluka chingauluke imakwana nthawi ndipo chimatera

M’dima ukure bwanji kunja kungade bwanji koma kumaera iwe dikilabe

Mavuto achuluke osatenga chingwe kuchosa moyo wako iwe pempherabe

Maso a Yehova amaona ponse khutu lake silogotha iwe pempherabe

Pamene wathedwa mzeru wasowa mtengo ogwira chisomo chimaoneka iwe pempherabe

Analonjeza mdalitso kwa onse okhulupilira omwe ndi ana ake adzawadalitsa

Uuuuuuuuuuuuuuuuu

Chorus

Follow Us

More Songs From Loyce yotamu

malawigospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel Music and any gospel News.malawigospelmusic.com offer services like song lyrics,Audio upload,poems,Music video upload on our You Tube channel called Malawian Gospel Music, Artist biography, Extended playlist (EP),Article, Album and Banner on website. For inquiry contact these numbers 0888 069 117/0885 572 836 or 0983 592 032/0994 56 15 46 or info@malawigospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media