Home » KUMUDZIWA_AIBOW_BANDA (AIBOW B)

KUMUDZIWA_AIBOW_BANDA (AIBOW B)

by Harris Msosa
187 views

Albow Banda yemwe amadziwika bwino ndi dzina lakuti Albow B pamayimbidwe anabadwa mu chaka cha 1988 ndipo m’banja mwawo anabadwa ana anayi ndipo iye ndi oyamba kubadwa.

Albow anayamba kuyimba m’chaka cha 2011 ndipo kufikira pano ali ndi zimbale zitatu monga Ndi Yesu Ameneyi, Mwamanga Pachani? komanso Ayoba ndipo pakatipa watulutsa nyimbo zina zatsopano zomwe zilipo 6 ndipo mayina a nyimbozo ndi monga Ndaimika Kaye, Come and see, Jerusalem iwe, Azakupeza uli pamwamba , Achulukilenji? komanso Dance and Joy.

AIbow amachokela ku Nguludi m’mudzi mwa Mataka T,A Likoswe m’boma la Chiladzulo ndipo pakadali pano akukhalira m’dziko la South Africa.

Spread the love

Follow Us

More Songs From Kumudziwa_aibow_banda (aibow

Leave a Comment

malawigospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel Music and any gospel News.malawigospelmusic.com offer services like song lyrics,Audio upload,poems,Music video upload on our You Tube channel called Malawian Gospel Music, Artist biography, Extended playlist (EP),Article, Album and Banner on website. For inquiry contact these numbers 0888 069 117/0885 572 836 or 0983 592 032/0994 56 15 46 or info@malawigospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media