-
Born on 9th April 1982 at queens Elizabeth Hospital in Blantyre,Martin Lyton Came into Public eye with his hit song titled Tatulukako kuiguputo in 2017.Second born son in a family …
-
Chrispine Chaoneka nde dzina lake lapamsonkho koma lapa stage ndi EL DEEZ.Khili adabadwila ku Lilongwe, likuni hospital pa 18 February 1985 ndipo ndiwachiwili kubadwa m’banja la ana atatu.Oyamba kubadwa ndi …
-
Juliet Kunje Kazipeze anabadwira ku Bangwe mu mzinda wa Blantyre pa 10 March 1987, koma kumudzi kwawo ndi kwa Chitera ku Chiladzuru,ndipo m’banja mwawo anabadwa ana 4 iye ndi wa …
-
Platson Keliam Chammudzi anabadwa ndi kukulira ku Neno m’mudzi wa amtemankhawa T/A Dambe.Platson anabadwa pa 5/01/1994 ndipo m’banja mwawo anabadwa ana 8 anatsala amoyo 7 m’modzi adamwalira ndipo iye ndi …
-
King William Chirwa Contacts:0996091516/0885606368 King William Chirwa Anabadwila ku Kasungu, Mtunthama trading center, T.A Wimbe. Anabadwa pa 18 January 1993 mu banja la ana 7 , anyamata 5 , atsikana …
-
Edward Filipo is a Malawian by nationality from Chewa tribe southern region of Malawi,Mangochi district.He was born in the family of 10 children,5 boys and 5 girls and he is …
-
Elisha Mbendera ndilo dzina lake lapa msonkho.Anabadwa mu chaka cha 1987 ndipo amakondwerera tsiku lakubadwa kwake pa 6 september. Anabadwa m’banja la Bambo ndi Mayi Mbendera pomwe anabereka ana okwana …
-
Clement Maungena “BK Boy” born on 12 September 1982 in Machinga district. He is from Balaka district, Batamila 2, T\A Nsamala. He is a Mechanical engineer and a musician and …
-
James Gulule ndi woimba,mtumiki (Evangelist) komanso mphunzitsi yemwe adabadwa pa 4 April,1992.Ndi mwana woyamba kubadwa m’banja la kwawo momwe muli ana 9 (amuna 4 ndipo akazi 5).Ndiokwatira ndipo ali ndi …
-
Camillius Simakweri anabadwila ku chileka m’boma la Blantyre ndipo anakulira ku Zimbabwe komwe anachita maphunziro ake a primary.Banja la kwawo anabadwa ana atatu ( kumbali ya amayi )ndipo ana 5 …
-
The group is based in Liwonde township in Machinga district. The group started in 2016 and by then made a collaboration with Liwonde Christ Ambassadors Choir under Malawi Assemblies of …
-
Cephas Kachingwe amachokela kwa T/A Ganya m’mudzi mwa chimowa m’boma la Ntcheu ndipo anabadwa pa 05-12-1983, iye ndi mwana wa chiwiri m’banja lomwe munabadwaso ana awiri.Pakadali pano amakhala ku Lilongwe …
-
Mabvuto Panganani anabadwa mu Chaka cha 1982 mu banja la ana 4 mwa ana atatu ndi akazi wamamuna alipo yekha komanso wotsiliza pobadwa woyamba kubadwa ndi Teleza kenako Tikalipo ndikubwera …
-
Lameck Soko was born on 7th April,1975 in the City of Blantyre at QueenElizabeth Central Hospital (Q.E.C.H) He is from Semion Mvula Village, T / A Mbelwa V, in Mzimba. …
All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media